top of page

ACHINYAMATA A MPINGO WA MTUNTHAMA AGAWA MABUKU 100

Writer's picture: J. MaclayJ. Maclay

Achinyamata a mpingo wa Mtunthama pa 17 August 2024 anali ndi Chilinganizo Chogawa mabuku (Street Evangelism).


Chilinganizochi chinatsogodzedwa ndi atsogoleri a pa mpingowu.


Master Guide Tinyade Massi ndi Master Guide Hamphery Namakhusa analimbikitsa achinyamata onse kuti akuyenera kunyamuka kupita kukafalitsa uthenga wa Mulungu ( I will go).


Ulendo ogawa mabuku unayambila pa Puma filing Station , St Andrews Trading centre ,mtunthama trading centre ,komboni ya French kukamalizila pa msika.


Achinyamatawa atha kukwanitsa kugawa mabuku 100 , ( Chiyembekezo Chotsiriza ,Signs of Hope komanso ma pepala a VOP kwa abale ndi alongo onse omwe anakumana nawo .


Mu ulendo onsewu, mkulu wa mpingo Charles Chikuni ndi omwe adalalikira mmadera onse.


Lucas Henry

CMC Media

 
 

Commentaires


About CMC 

Welcome to Central Malawi Conference of the Seventh-day Adventist Church in Malawi!

 

On behalf of the 118,712 plus Seventh-day Adventists who comprise Central Malawi Conference of the Seventh-day Adventist Church in Malawi, I congratulate you for visiting our website. We are here to serve you. Central Malawi Conference started out as a mission field in 1964 and was first headquartered at Dedza Boma some 99 kilometers from Lilongwe and about 221 kilometers from Blantyre off the M1 road in Malawi.  Read More

Explore GUMA

Classmates

 JOIN 
Adventist
Children
Ministries

CONTACT US            

 

Kaunda Road - Area 49, Next to Area 49 SDA Church, Lilongwe.

 

Mail: Private Bag B-516 Capital City, Lilongwe 3, Malawi.

Phone: 265-177-9100;  265-177-9101, Fax: +265-177-3814. 

Email: info@cmc.adventist.org

MISSION             

“To spread the everlasting gospel in the context of the three angels messages of Revelation 14:6-12 to all the people of the Central Region of Malawi”

VISION                                  

 

A Conference that disciples all in the Central Region of Malawi.”

bottom of page